Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 13:29 - Buku Lopatulika

29 chomwecho inunso, pamene muona zinthu izi zilikuchitika, zindikirani kuti ali pafupi pakhomo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 chomwecho inunso, pamene muona zinthu izi zilikuchitika, zindikirani kuti ali pafupi pakhomo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Momwemonso mukadzaona zija ndanenazi zikuchitika, mudzadziŵe kuti Mwana wa Munthu ali pafupi, ali pakhomo penipeni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Momwenso pamene muona zinthu izi zikuchitika, dziwani kuti wayandikira, ali pa khomo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:29
7 Mawu Ofanana  

Ndipo phunzirani ndi mkuyu fanizo lake; pamene pafika kuti nthambi yake ikhala yanthete, ndipo anaphuka masamba ake, muzindikira kuti layandikira dzinja;


Indetu ndinena ndi inu, Mbadwo uno sudzapita kufikira zinthu izi zonse zitachitika.


Musaipidwe wina ndi mnzake, abale, kuti mungaweruzidwe. Taonani, woweruza aima pakhomo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa