Marko 13:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo pamenepo adzaona Mwana wa Munthu alinkudza m'mitambo ndi mphamvu yaikulu, ndi ulemerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo pamenepo adzaona Mwana wa Munthu alinkudza m'mitambo ndi mphamvu yaikulu, ndi ulemerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Pamenepo anthu adzaona Mwana wa Munthu akubwera pa mitambo, ali ndi mphamvu zazikulu ndi ulemerero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 “Nthawi imeneyo anthu adzaona Mwana wa Munthu akubwera mʼmitambo ndi mphamvu yayikulu ndi ulemerero. Onani mutuwo |