Marko 13:17 - Buku Lopatulika17 Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana masiku awo! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma tsoka iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana masiku awo! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ali ndi tsoka akazi amene adzakhale ndi pathupi, ndiponso azimai oyamwitsa ana masiku amenewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kudzakhala koopsa mʼmasiku amenewo kwa amayi oyembekezera ndi amayi oyamwitsa! Onani mutuwo |