Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 13:15 - Buku Lopatulika

15 ndi iye amene ali pamwamba pa tsindwi asatsike, kapena asalowe kukatulutsa kanthu m'nyumba mwake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndi iye amene ali pamwamba pa chindwi asatsike, kapena asalowe kukatulutsa kanthu m'nyumba mwake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Amene ali padenga pa nyumba yake, asati atsike kuti akatenge chinthu m'nyumba mwakemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Aliyense amene ali pa denga la nyumba yake asatsike kapena kulowa mʼnyumba kukatenga kanthu kalikonse.

Onani mutuwo Koperani




Marko 13:15
13 Mawu Ofanana  

Fulumira, thawira kumeneko; pakuti sindithai kuchita kanthu usadafike kumeneko. Chifukwa chake anatcha dzina la mzindawo Zowari.


Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.


Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Khungu kulipa khungu, inde munthu adzapereka zonse ali nazo kuombola moyo wake.


Wochenjera aona zoipa, nabisala; koma achibwana angopitirira, nalipitsidwa.


ndi iye amene ali kumunda asabwere kudzatenga malaya ake.


Ndipo m'mene anakhuta, anapepuza ngalawa, nataya tirigu m'nyanja.


Ndi chikhulupiriro Nowa, pochenjezedwa ndi Mulungu za zinthu zisanapenyeke, ndi pochita mantha, anamanga chingalawa cha kupulumutsiramo iwo a m'nyumba yake; kumene anatsutsa nako dziko lapansi, nakhala wolowa nyumba wa chilungamo chili monga mwa chikhulupiriro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa