Marko 12:40 - Buku Lopatulika40 amenewo alusira nyumba za akazi amasiye, napemphera monyenga mau ambiri; amenewa adzalandira kulanga koposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 amenewo alusira nyumba za akazi amasiye, napemphera monyenga mau ambiri; amenewa adzalandira kulanga koposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Koma amaŵadyera chuma chao azimai amasiye, nkumapemphera mapemphero ataliatali monyengezera. Anthu ameneŵa adzalangidwa koposa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Amawononga chuma cha akazi amasiye ndiponso amapemphera mapemphero aatali odzionetsera. Anthu oterewa adzalangidwa kwambiri.” Onani mutuwo |