Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:39 - Buku Lopatulika

39 ndi kukhala nayo mipando yaulemu m'sunagoge, ndi malo aulemu pamaphwando:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 ndi kukhala nayo mipando yaulemu m'sunagoge, ndi malo aulemu pamaphwando:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Amakonda mipando yaulemu kwambiri m'nyumba zamapemphero, ndiponso malo olemekezeka pa maphwando.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Ndipo amakhala pa mipando yofunika kwambiri mʼmasunagoge ndi malo aulemu pa maphwando.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:39
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Yesu analankhula ndi makamu a anthu ndi ophunzira ake,


nakonda malo a ulemu pamaphwando, ndi mipando ya ulemu m'masunagoge,


Ndipo m'chiphunzitso chake ananena, Yang'anirani mupewe alembi, akufuna kuyendayenda ovala miinjiro, ndi kulonjeredwa pamisika,


amenewo alusira nyumba za akazi amasiye, napemphera monyenga mau ambiri; amenewa adzalandira kulanga koposa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa