Marko 12:31 - Buku Lopatulika31 Lachiwiri ndi ili, Uzikonda mnzako monga udzikonda mwini. Palibe lamulo lina lakuposa awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Lachiwiri ndi ili, Uzikonda mnzako monga udzikonda mwini. Palibe lamulo lina lakuposa awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Lamulo lachiŵiri lake ndi ili, ‘Uzikonda mnzako monga momwe umadzikondera iwe wemwe.’ Palibe lamulo lina loposa malamulo ameneŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Lachiwiri ndi ili: ‘Konda mnansi wako monga iwe mwini.’ Palibe lamulo lina loposa amenewa.” Onani mutuwo |