Marko 12:27 - Buku Lopatulika27 Sali Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: musochera inu ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Sali Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: musochera inu ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ndiye kutitu sali Mulungu wa anthu akufa ai, koma wa anthu amoyo. Inu ndinu olakwa kwabasi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iye si Mulungu wa anthu akufa, koma wa amoyo. Inu mwalakwitsa kwambiri!” Onani mutuwo |