Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:27 - Buku Lopatulika

27 Sali Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: musochera inu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Sali Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: musochera inu ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Ndiye kutitu sali Mulungu wa anthu akufa ai, koma wa anthu amoyo. Inu ndinu olakwa kwabasi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Iye si Mulungu wa anthu akufa, koma wa amoyo. Inu mwalakwitsa kwambiri!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:27
9 Mawu Ofanana  

Ukangofuna, mwananga, kusochera kusiya mau akudziwitsa, leka kumva mwambo.


Koma Yesu anayankha, nati kwa iwo, Mungolakwa osadziwa malembo, kapena mphamvu za Mulungu.


Ine ndili Mulungu wa Abrahamu, ndi Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo? Sali Mulungu wa akufa koma wa amoyo.


Yesu ananena nao, Simusochera nanga mwa ichi, popeza mulibe kudziwa malembo, kapena mphamvu yake ya Mulungu?


Ndipo Iye sakhala Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: pakuti anthu onse akhala ndi moyo kwa Iye.


Pakuti, chifukwa cha ichi Khristu adafera, nakhalanso ndi moyo, kuti Iye akakhale Ambuye wa akufa ndi wa amoyo.


monga kwalembedwa: Ndinakukhazika iwe kholo la mitundu yambiri ya anthu pamaso pa Mulungu amene iye anamkhulupirira, amene apatsa akufa moyo, ndi kuitana zinthu zoti palibe, monga ngati zilipo.


Momwemo ndinakwiya nao mbadwo uwu, ndipo ndinati, Nthawi zonse amasochera mumtima; koma sanazindikire njira zanga iwowa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa