Marko 12:25 - Buku Lopatulika25 Pakuti pamene adzauka kwa akufa, sakwatira, kapena sakwatiwa; koma akhala ngati angelo a Kumwamba. Koma za akufa, kuti akaukitsidwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pakuti pamene adzauka kwa akufa, sakwatira, kapena sakwatiwa; koma akhala ngati angelo a Kumwamba. Koma za akufa, kuti akaukitsidwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Pajatu pouka akufa, palibenso za kukwatira kapena kukwatiwa ai. Onse ali ngati angelo Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pamene akufa auka, sadzakwatira kapena kukwatiwa; adzakhala ngati angelo kumwamba. Onani mutuwo |