Marko 12:24 - Buku Lopatulika24 Yesu ananena nao, Simusochera nanga mwa ichi, popeza mulibe kudziwa malembo, kapena mphamvu yake ya Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Yesu ananena nao, Simusochera nanga mwa ichi, popeza mulibe kudziwa malembo, kapena mphamvu yake ya Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Yesu adaŵayankha kuti, “Si pamenepa nanga pomwe mumalakwira, chifukwa chosadziŵa Malembo ndiponso mphamvu za Mulungu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Yesu anawafunsa kuti, “Kodi si pamenepa nanga pomwe mumalakwira chifukwa simukudziwa malemba kapena mphamvu za Mulungu? Onani mutuwo |