Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 12:23 - Buku Lopatulika

23 Pakuuka adzakhala mkazi wa yani wa iwowa? Pakuti asanu ndi awiriwo adamuyesa mkazi wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Pakuuka adzakhala mkazi wa yani wa iwowa? Pakuti asanu ndi awiriwo adamuyesa mkazi wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Nanga tsono pa tsiku lodzauka akufa, mwini mkaziyo adzakhala utiwuti, popeza kuti abale asanu ndi aŵiri onse aja adaamkwatirapo?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Pa kuuka kwa akufa, adzakhala mkazi wa yani pakuti anakwatiwa ndi onse asanu ndi awiri?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:23
3 Mawu Ofanana  

Kondani Yehova, Inu nonse okondedwa ake, Yehova asunga okhulupirika, ndipo abwezera zochuluka iye wakuchita zodzitama.


ndipo asanu ndi awiriwo analibe kusiya mbeu. Potsiriza pake pa onse mkazinso anafa.


Yesu ananena nao, Simusochera nanga mwa ichi, popeza mulibe kudziwa malembo, kapena mphamvu yake ya Mulungu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa