Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:19 - Buku Lopatulika

19 Mphunzitsi, Mose anatilembera, kuti, Akafa mbale wake wa munthu, nasiya mkazi, wosasiya mwana, mbale wake atenge mkazi wake, namuukitsire mbale wakeyo mbeu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Mphunzitsi, Mose anatilembera, kuti, Akafa mbale wake wa munthu, nasiya mkazi, wosasiya mwana, mbale wake atenge mkazi wake, namuukitsire mbale wakeyo mbeu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 “Aphunzitsi, Mose adatilembera lamulo lakuti, ‘Ngati munthu amwalira, nasiya mkazi, koma opanda ana, mbale wake wa womwalirayo aloŵe chokolo, kuti amuberekere ana mbale wake uja.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Iwo anati, “Aphunzitsi, Mose anatilembera kuti munthu akamwalira ndi kusiya mkazi wopanda ana, mʼbale wa munthu womwalirayo akuyenera kukwatira mkaziyo kuti amuberekere ana mʼbale wakeyo.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yuda anati kwa Onani, Lowani naye mkazi wa mbale wako, ndi kumchitira mkazi zoyenera mphwake wa mwamuna wake, ndi kumuukitsira mkulu wako mbeu.


Analipo abale asanu ndi awiri; woyamba anakwatira mkazi, nafa, wosasiya mbeu;


Potero m'kuuka iye adzakhala mkazi wa yani wa iwo? Pakuti asanu ndi awiriwo adamkwatira iye.


Nati Bowazi, Tsiku lomwelo ugula mundawo padzanja la Naomi, uugulanso kwa Rute, Mmowabu, mkazi wa wakufayo, kuukitsira dzina la wakufayo pa cholowa chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa