Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 12:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anadza kwa Iye Asaduki, amene amanena kuti palibe kuuka kwa akufa; ndipo anamfunsa Iye, nanena,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anadza kwa Iye Asaduki, amene amanena kuti palibe kuuka kwa akufa; ndipo anamfunsa Iye, nanena,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pambuyo pake Asaduki ena adadza kwa Yesu. Iwo amati akufa sadzauka. Adamufunsa kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Kenaka Asaduki, amene amati kulibe kuuka kwa akufa, anabwera kwa Iye ndi funso.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:18
6 Mawu Ofanana  

ndiwo amene adasokera kunena za choonadi, ponena kuti kuuka kwa akufa kwachitika kale, napasula chikhulupiriro cha ena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa