Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 11:30 - Buku Lopatulika

30 Ubatizo wa Yohane uchokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu? Mundiyankhe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ubatizo wa Yohane uchokera Kumwamba kodi, kapena kwa anthu? Mundiyankhe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Kodi Yohane kuti azibatiza, mphamvu zake adaazitenga kwa yani, kwa Mulungu kapena kwa anthu? Tandiyankhani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ubatizo wa Yohane, unali wochokera kumwamba, kapena kwa anthu? Ndiwuzeni.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:30
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ndikufunsani mau amodzi, mundiyankhe Ine, ndipo ndidzakuuzani ulamuliro umene ndichita nao zinthu zimenezi.


Ndipo anatsutsana mwa iwo okha, nanena, Tikati, Kumwamba; adzanena Iye, Ndipo simunakhulupirire iye bwanji?


Koma ndinena ndi inu kuti anafikadi Eliya, ndipo anamchitiranso zilizonse iwo anazifuna, monga kwalembedwa za iye.


Ndipo tsopano ndinena ndi inu, Lekani anthu amenewa, nimuwalole akhale; pakuti ngati uphungu umene kapena ntchito iyi ichokera kwa anthu, idzapasuka;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa