Marko 11:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ndikufunsani mau amodzi, mundiyankhe Ine, ndipo ndidzakuuzani ulamuliro umene ndichita nao zinthu zimenezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ndikufunsani mau amodzi, mundiyankhe Ine, ndipo ndidzakuuzani ulamuliro umene ndichita nao zinthu zimenezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adati, “Nanenso ntakufunsani funso limodzi. Mukandiyankha, ndiye ndikuuzeni kumene ndidatenga mphamvu zoti ndizichita zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Yesu anayankha kuti, “Ndikufunsani funso limodzi. Mundiyankhe, ndipo ndikuwuzani ndi ulamuliro wanji umene ndikuchitira izi. Onani mutuwo |