Marko 11:28 - Buku Lopatulika28 nanena naye, Izi muzichita ndi ulamuliro wotani? Kapena anakupatsani ndani ulamuliro uwu wakuchita izi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 nanena naye, Izi muzichita ndi ulamuliro wotani? Kapena anakupatsani ndani ulamuliro uwu wakuchita izi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 “Kodi mphamvu zoti muzichita zimenezi mudazitenga kuti? Ndani adakupatsani mphamvu zimenezi?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Iwo anafunsa kuti, “Mukuchita izi ndi ulamuliro wanji? Ndipo anakupatsani ulamuliro umenewu ndi ndani?” Onani mutuwo |