Marko 11:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo iwo anadzanso ku Yerusalemu; ndipo m'mene Iye anali kuyenda mu Kachisi, anafika kwa Iye ansembe aakulu, ndi alembi ndi akulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo iwo anadzanso ku Yerusalemu; ndipo m'mene Iye anali kuyenda m'Kachisi, anafika kwa Iye ansembe aakulu, ndi alembi ndi akulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Yesu adafikanso ku Yerusalemu. Tsono pamene Iye ankangodziyendera m'Nyumba ya Mulungu, akulu a ansembe ndi aphunzitsi a Malamulo pamodzi ndi akulu a Ayuda adadzamufunsa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iwo anafikanso ku Yerusalemu, ndipo pamene Yesu amayenda mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu, akulu a ansembe, aphunzitsi amalamulo ndi akuluakulu anabwera kwa Iye. Onani mutuwo |