Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 11:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anafika iwo ku Yerusalemu; ndipo Iye analowa mu Kachisi, nayamba kutulutsa akugulitsa ndi akugula malonda mu Kachisimo, nagubuduza magome a osinthana ndalama, ndi mipando ya ogulitsa nkhunda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anafika iwo ku Yerusalemu; ndipo Iye analowa m'Kachisi, nayamba kutulutsa akugulitsa ndi akugula malonda m'Kachisimo, nagubuduza magome a osinthana ndalama, ndi mipando ya ogulitsa nkhunda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Iwo adafika ku Yerusalemu. Tsono Yesu adaloŵa m'Nyumba ya Mulungu, nayamba kutulutsa anthu amene ankachita malonda m'menemo. Adagubudula matebulo a osinthitsa ndalama, ndi mipando ya ogulitsa nkhunda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Atafika ku Yerusalemu, Yesu analowa mʼbwalo lakunja la Nyumba ya Mulungu ndipo anayamba kupirikitsa anthu amene amagula ndi kugulitsa mʼmenemo. Anagubuduza matebulo a osintha ndalama ndi mipando ya ogulitsa nkhunda,

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:15
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anayankha nanena ndi uwo, Munthu sadzadyanso zipatso zako nthawi zonse. Ndipo ophunzira ake anamva.


ndipo sanalole munthu aliyense kunyamula chotengera kupyola pakati pa Kachisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa