Marko 10:50 - Buku Lopatulika50 Ndipo iye anataya chofunda chake, nazunzuka, nadza kwa Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Ndipo iye anataya chofunda chake, nazunzuka, nadza kwa Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Pomwepo iye uja adadzambatuka, mwinjiro wake uko chi, kuthamangira kwa Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Anaponya mkanjo wake kumbali, analumpha nabwera kwa Yesu. Onani mutuwo |