Marko 10:48 - Buku Lopatulika48 Ndipo ambiri anamulamula kuti atonthole: koma makamaka anafuulitsa kuti, Inu mwana wa Davide, mundichitire chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ndipo ambiri anamulamula kuti atonthole: koma makamaka anafuulitsa kuti, Inu mwana wa Davide, mundichitire chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Anthu ambiri adamzazira kuti akhale chete. Koma iye adafuulirafuulira kuti, “Inu Mwana wa Davide, mundichitire chifundo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Ambiri anamukalipira ndi kumuwuza kuti akhale chete, koma iye anafuwulitsabe kuti, “Mwana wa Davide, mundichitire chifundo!” Onani mutuwo |