Marko 10:40 - Buku Lopatulika40 koma kukhala kudzanja langa lamanja, kapena lamanzere sikuli kwanga kupatsa; koma kuli kwa iwo amene adawakonzeratu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 koma kukhala kudzanja langa lamanja, kapena lamanzere sikuli kwanga kupatsa; koma kuli kwa iwo amene adawakonzeratu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Koma Ineyo si udindo wanga kusankha munthu kuti akhale ku dzanja langa lamanja, kapena ku dzanja langa lamanzere. Mulungu ndiye adzapereke malo ameneŵa kwa omwe Iye mwini adaŵakonzera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 koma kukhala kumanja kapena kumanzere si Ine wopereka. Malo awa ndi a amene anasankhidwiratu.” Onani mutuwo |