Marko 10:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo iwo anati kwa Iye, Mutipatse ife kuti tikhale mmodzi kudzanja lanu lamanja, ndi wina kulamanzere, mu ulemerero wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo iwo anati kwa Iye, Mutipatse ife kuti tikhale mmodzi kudzanja lanu lamanja, ndi wina kulamanzere, m'ulemerero wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Iwo adati, “Timafuna kuti pamene mudzakhale mu ulemerero wanu, mudzatiike wina ku dzanja lanu lamanja, wina ku dzanja lanu lamanzere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Iwo anayankha kuti, “Timafuna kuti mmodzi wa ife adzakhale kumanja ndi wina kumanzere mu ulemerero wanu.” Onani mutuwo |