Marko 10:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo Iye anati kwa iwo, Mufuna kuti ndidzakuchitireni inu chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo Iye anati kwa iwo, Mufuna kuti ndidzakuchitireni inu chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Yesu adaŵafunsa kuti, “Inuyo mukufuna kuti ndikuchitireni chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Iye anafunsa kuti, “Kodi mukufuna ndikuchitireni chiyani?” Onani mutuwo |