Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 10:31 - Buku Lopatulika

31 Koma ambiri akuyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Koma ambiri akuyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Komatu ambiri amene ali oyambirira adzakhala otsirizira, ndipo amene ali otsirizira adzakhala oyambirira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Koma ambiri amene ndi woyambirira adzakhala omalizira, ndipo omalizira adzakhala oyambirira.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:31
10 Mawu Ofanana  

Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.


Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Ndani wa awiriwo anachita chifuniro cha atate wake? Iwo ananena, Woyambayo. Yesu ananena kwa iwo, Indetu ndinena kwa inu, kuti amisonkho ndi akazi achiwerewere amatsogolera inu, kulowa mu Ufumu wa Kumwamba.


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa