Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 10:28 - Buku Lopatulika

28 Petro anayamba kunena naye, Onani, ife tinasiya zonse, ndipo tinakutsatani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Petro anayamba kunena naye, Onani, ife tinasiya zonse, ndipo tinakutsatani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Pamenepo Petro adayamba kulankhula naye, adati, “Ifetu paja tidasiya zonse kuti tizikutsatani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Petro anati kwa Iye, “Ife tasiya zonse ndi kukutsatani!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:28
9 Mawu Ofanana  

mphindi yakufunafuna ndi mphindi yakumwazika; mphindi yakusunga ndi mphindi yakutaya;


Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.


Ndipo anasiya pomwepo ngalawayo ndi atate wao, namtsata Iye.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Chifukwa chake tsono, yense wa inu amene sakaniza zonse ali nazo, sangathe kukhala wophunzira wanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa