Marko 10:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo iye anati kwa Iye, Mphunzitsi, zonsezi ndinazisunga kuyambira ndili mwana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo iye anati kwa Iye, Mphunzitsi, zonsezi ndinazisunga kuyambira ndili mwana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Munthu uja adati, “Aphunzitsi, zonsezi ndakhala ndikuzitsata kuyambira ndili mwana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anati, “Aphunzitsi zonsezi ndinazisunga kuyambira ndili mnyamata.” Onani mutuwo |