Marko 10:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino koma mmodzi, ndiye Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino koma mmodzi, ndiye Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Yesu adamuyankha kuti, “Ukunditchuliranji wabwino? Wabwinotu ndi mmodzi yekha, Mulungu basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Yesu anamufunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani ukunditchula wabwino? Palibe wabwino koma Mulungu yekha. Onani mutuwo |