Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 1:37 - Buku Lopatulika

37 nampeza, nanena naye, Akufunani Inu anthu onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 nampeza, nanena naye, Akufunani Inu anthu onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Atampeza adamuuza kuti, “Anthu onse akukufunafunani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 ndipo atamupeza, anamuwuza kuti, “Aliyense akukufunani!”

Onani mutuwo Koperani




Marko 1:37
7 Mawu Ofanana  

Ndipo linathyoka tsikulo, momwemo zonyankhalala za zoweta, zakundisamalira Ine, zinadziwa kuti ndiwo mau a Yehova.


Ndipo Simoni ndi anzake anali naye anamtsata,


Ndipo ananena nao, Tiyeni kwina, kumidzi ili pafupi apa, kuti ndilalikire komwekonso; pakuti ndadzera ntchito imeneyi.


Ndipo anatuluka a ku dziko lonse la Yudeya, ndi a ku Yerusalemu onse; nadza kwa iye nabatizidwa ndi iye mumtsinje Yordani, powulula machimo ao.


Ngati timleka Iye kotero, onse adzakhulupirira Iye; ndipo adzadza Aroma nadzachotsa malo athu ndi mtundu wathu.


Chifukwa chake Afarisi ananena wina ndi mnzake, Muona kuti simupindula kanthu konse; onani dziko litsata pambuyo pake pa Iye.


Ndipo anadza kwa Yohane, nati kwa iye, Rabi, Iye amene anali ndi inu tsidya lija la Yordani, amene munamchitira umboni, taonani yemweyu abatiza, ndipo anthu onse alinkudza kwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa