Marko 1:37 - Buku Lopatulika37 nampeza, nanena naye, Akufunani Inu anthu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 nampeza, nanena naye, Akufunani Inu anthu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Atampeza adamuuza kuti, “Anthu onse akukufunafunani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 ndipo atamupeza, anamuwuza kuti, “Aliyense akukufunani!” Onani mutuwo |