Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 1:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo mzinda wonse unasonkhana pakhomo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo mudzi wonse unasonkhana pakhomo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Anthu a m'mudzi monsemo adaasonkhana pakhomopo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Anthu onse a mʼmudzimo anasonkhana pa khomo,

Onani mutuwo Koperani




Marko 1:33
4 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo analowa mu Kapernao; ndipo pomwepo pa tsiku la Sabata iye analowa m'sunagoge naphunzitsa.


Ndipo anachiritsa anthu ambiri akudwala nthenda za mitundumitundu, natulutsa ziwanda zambiri; ndipo sanalole ziwandazo zilankhule, chifukwa zinamdziwa Iye.


Ndipo anatuluka a ku dziko lonse la Yudeya, ndi a ku Yerusalemu onse; nadza kwa iye nabatizidwa ndi iye mumtsinje Yordani, powulula machimo ao.


Ndipo Sabata linalo udasonkhana pamodzi ngati mzinda wonse kumva mau a Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa