Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 1:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Mwamsanga mbiri yake idawanda ponseponse ku dera lonse la ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Mbiri yake inafalikira kudera lonse la Galileya mofulumira.

Onani mutuwo Koperani




Marko 1:28
10 Mawu Ofanana  

Ndipo adzaimirira, nadzadyetsa nkhosa zake mu mphamvu ya Yehova, mu ukulu wa dzina la Yehova Mulungu wake; ndipo iwo adzakhalabe; pakuti pamenepo Iye adzakhala wamkulu kufikira malekezero a dziko lapansi.


Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


Ndipo mbiri yake imene inabuka m'dziko lonse limenelo.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Ndipo anazizwa onse, kotero kuti anafunsana mwa iwo okha, kuti, Ichi nchiyani? Chiphunzitso chatsopano! Ndi mphamvu alamula ingakhale mizimu yonyansa, ndipo imvera Iye.


Ndipo pomwepo, potuluka m'sunagoge, iwo analowa m'nyumba ya Simoni ndi Andrea pamodzi ndi Yakobo ndi Yohane.


Koma iye anatuluka nayamba kulalikira ndithu, ndi kubukitsa mauwo, kotero kuti Yesu sanathe kulowanso poyera m'mudzi, koma anakhala padera m'mapululu; ndipo anadza kwa Iye anthu a kumalo onse.


Ndipo anapereka kwa Iye buku la Yesaya mneneri. Ndipo m'mene Iye adafunyulula bukulo, anapeza pomwe panalembedwa,


Ndipo mbiri yake ya Iye inafalikira kumalo onse a dziko loyandikira.


Ndipo mbiri yake imeneyo inabuka ku Yudeya yense, ndi ku dziko lonse loyandikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa