Marko 1:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo mbiri yake inabuka pompaja kudziko lonse la Galileya lozungulirapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Mwamsanga mbiri yake idawanda ponseponse ku dera lonse la ku Galileya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Mbiri yake inafalikira kudera lonse la Galileya mofulumira. Onani mutuwo |