Maliro 5:6 - Buku Lopatulika6 Tinagwira mwendo Ejipito ndi Asiriya kuti tikhute zakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Tinagwira mwendo Ejipito ndi Asiriya kuti tikhute zakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tidachita chibwenzi ndi Aejipito ndiponso ndi Aasiriya, kuti mwina iwo nkutipatsako chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tinadzipereka kwa Aigupto ndi kwa Asiriya kuti tipeze chakudya. Onani mutuwo |