Maliro 5:5 - Buku Lopatulika5 Otilondola atigwira pakhosi pathu, tatopa osaona popumira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Otilondola atigwira pakhosi pathu, tatopa osaona popumira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Amatikankha mwankhanza, goli lili m'khosi mwathu. Ngakhale titope, satilola kupumula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Otilondola atigwira pakhosi; tafowoka ndipo sakutilola kupumula. Onani mutuwo |