Maliro 5:12 - Buku Lopatulika12 Anawapachika akalonga manja ao; sanalemekeze nkhope za akulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Anawapachika akalonga manja ao; sanalemekeze nkhope za akulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Akalonga akuŵapachika pomangirira manja ao, akuluakulu sakuŵalemekeza konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Akalonga athu akuwapachika pomangirira manja awo, akuluakulu sakuwalemekeza. Onani mutuwo |