Maliro 5:11 - Buku Lopatulika11 Anaipitsa akazi mu Ziyoni, ndi anamwali m'midzi ya Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Anaipitsa akazi m'Ziyoni, ndi anamwali m'midzi ya Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ku Ziyoni akazi akuŵachita zadama mwakhakhamizo. M'mizinda ina ya ku Yuda anamwali akuŵachita chimodzimodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Amayi agwiriridwa mu Ziyoni, ndi anamwali mʼmizinda ya Yuda. Onani mutuwo |