Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 5:10 - Buku Lopatulika

10 Khungu lathu lapserera ngati pamoto chifukwa cha kuwawa kwa njala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Khungu lathu lapserera ngati pamoto chifukwa cha kuwawa kwa njala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Khungu lathu likutentha ngati lili m'ng'anjo chifukwa cha ululu wa njala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Khungu lathu latentha ngati uvuni mʼngʼanjo, chifukwa cha kuwawa kwa njala.

Onani mutuwo Koperani




Maliro 5:10
4 Mawu Ofanana  

Khungu langa lada, nilindifundukira; ndi mafupa anga awawa ndi kutentha kwao.


Popeza ndakhala ngati thumba lofukirira; koma sindiiwala malemba anu.


Wagugitsa thupi langa ndi khungu langa, nathyola mafupa anga.


Maonekedwe ao ada koposa makala, sazindikirika m'makwalala; khungu lao limamatira pa mafupa ao, lakhwinyata, lasanduka ngati ndodo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa