Maliro 4:7 - Buku Lopatulika7 Omveka ake anakonzeka koposa chipale chofewa, nayera koposa mkaka, matupi ao anafiira koposa timiyala toti psu; maonekedwe ao ananga a safiro wa mtengo wapatali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Omveka ake anakonzeka koposa chipale chofewa, nayera koposa mkaka, matupi ao anafiira koposa timiyala toti psu; maonekedwe ao ananga a safiro wa mtengo wapatali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Akalonga ake anali oŵala koposa chisanu chambee, oyera kuposa mkaka. Matupi ao anali ofiira kupambana miyala ya rubi. Anali ndi maonekedwe okongola ngati miyala ya safiro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Akalonga ake anali owala koposa chisanu chowundana ndi oyera kuposa mkaka. Matupi awo anali ofiira kuposa miyala ya rubi, maonekedwe awo ngati miyala ya safiro. Onani mutuwo |