Maliro 4:13 - Buku Lopatulika13 Ndicho chifukwa cha machimo a aneneri ndi mphulupulu za ansembe ake, amene anakhetsa mwazi wa olungama pakati pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndicho chifukwa cha machimo a aneneri ndi mphulupulu za ansembe ake, amene anakhetsa mwazi wa olungama pakati pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Zimenezi zidachitika chifukwa cha machimo a aneneri ake ndi ntchito zoipa za ansembe ake, amene ankakhetsa magazi a anthu osalakwa m'malinga amumzindamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma izi zinachitika chifukwa cha kuchimwa kwa aneneri ake ndi mphulupulu za ansembe ake, amene ankapha anthu osalakwa pakati pawo. Onani mutuwo |