Maliro 4:11 - Buku Lopatulika11 Yehova wakwaniritsa kuzaza kwake, watsanulira ukali wake; anayatsa moto mu Ziyoni, unanyambita maziko ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova wakwaniritsa kuzaza kwake, watsanulira ukali wake; anayatsa moto m'Ziyoni, unanyambita maziko ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adakwiya kwambiri, nagwetsa pansi mkwiyo wake wamotowo. Adayatsa moto ku Ziyoni ndipo motowo udaononga maziko a mzindawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova wakwaniritsa ukali wake; wagwetsa pansi mkwiyo wake woopsa. Ndipo wayatsa moto mʼZiyoni kuti uwononge maziko ake. Onani mutuwo |