Maliro 3:7 - Buku Lopatulika7 Wanditsekereza ndi guta, sindingatuluke; walemeretsa unyolo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Wanditsekereza ndi guta, sindingatuluke; walemeretsa unyolo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adanditsekera m'malinga kuti ndisathaŵe. Adandimanga ndi maunyolo olemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe, wandimanga ndi maunyolo. Onani mutuwo |