Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:53 - Buku Lopatulika

53 anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwamba pa ine;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwamba pa ine;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Adandiponya m'dzenje ndili moyo, nkumandiponya miyala ndili momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje ndi kundiponya miyala;

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:53
9 Mawu Ofanana  

Atafika Yeremiya kunyumba yadzenje, ku tizipinda take nakhalako Yeremiya masiku ambiri;


Tsopano tamvanitu, mbuyanga mfumu; pembedzero langa ligwe pamaso panu; kuti musandibwezere kunyumba ya Yonatani mlembi, ndingafe kumeneko.


Ndipo anatenga Yeremiya, namponya iye m'dzenje la Malikiya mwana wake wa mfumu, limene linali m'bwalo la kaidi; ndipo anamtsitsa Yeremiya ndi zingwe. Koma m'dzenjemo munalibe madzi, koma thope; namira Yeremiya m'thopemo.


Mbuyanga mfumu, anthu awa anachita zoipa m'zonse anachitira Yeremiya mneneri, amene anamponya m'dzenje; ndipo afuna kufa m'menemo chifukwa cha njala; pakuti mulibe chakudya china m'mzindamu.


Ndipo anatenga mwala, nauika pakamwa pa dzenje, niukomera mfumu ndi chosindikizira chake, ndi chosindikizira cha akulu ake, kuti kasasinthike kanthu ka Daniele.


Pamenepo mfumu inamuka kuchinyumba chake, nichezera kusala usikuwo, ngakhale zoimbitsa sanabwere nazo pamaso pake, ndi m'maso mwake munamuumira.


Pamenepo Yona anapemphera kwa Yehova Mulungu wake ali m'mimba mwa nsombayo.


nauika m'manda ake atsopano, osemedwa m'mwala, nakunkhunizira mwala waukulu pakhomo pa manda, nachokapo.


Ndipo iwo anamuka, nasunga manda, nasindikizapo chizindikiro pamwalapo, iwo pamodzi ndi alondawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa