Maliro 3:53 - Buku Lopatulika53 anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwamba pa ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwamba pa ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Adandiponya m'dzenje ndili moyo, nkumandiponya miyala ndili momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje ndi kundiponya miyala; Onani mutuwo |