Maliro 3:52 - Buku Lopatulika52 Ondida opanda chifukwa anandiinga ngati mbalame; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Ondida opanda chifukwa anandiinga ngati mbalame; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Amene anali adani anga popanda chifukwa, akhala akundisaka ngati mbalame. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Akundisaka ngati mbalame, amene anali adani anga, popanda chifukwa. Onani mutuwo |