Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:52 - Buku Lopatulika

52 Ondida opanda chifukwa anandiinga ngati mbalame;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 Ondida opanda chifukwa anandiinga ngati mbalame;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 Amene anali adani anga popanda chifukwa, akhala akundisaka ngati mbalame.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 Akundisaka ngati mbalame, amene anali adani anga, popanda chifukwa.

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:52
15 Mawu Ofanana  

Ndipo anandizinga ndi mau a udani, nalimbana nane kopanda chifukwa.


Ndakhulupirira Yehova, mutani nkunena kwa moyo wanga, Thawirani kuphiri lanu ngati mbalame?


Nduna zinandilondola kopanda chifukwa; koma mtima wanga uchita nao mantha mau anu.


Moyo wathu unaonjoka ngati mbalame mu msampha wa msodzi; msampha unathyoka ndi ife tinaonjoka.


Adani anga asandikondwerere ine monyenga; okwiya nane kopanda chifukwa asanditsinzinire.


Pakuti ananditchera ukonde wao m'mbunamo kopanda chifukwa, anakumbira moyo wanga dzenje kopanda chifukwa.


Ondida kopanda chifukwa achuluka koposa tsitsi la pamutu panga; ofuna kunditha, ndiwo adani anga monama, ali ndi mphamvu. Pamenepo andibwezetsa chosafunkha ine.


Ndipo Yeremiya anati kwa mfumu Zedekiya, Ndachimwira inu chiyani, kapena atumiki anu, kapena anthu awa, kuti mwandiika m'nyumba yandende?


Diso langa limvetsa moyo wanga zowawa chifukwa cha ana aakazi onse a m'mzinda mwanga.


Koma chitero, kuti mau olembedwa m'chilamulo chao akwaniridwe, kuti, Anandida Ine kopanda chifukwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa