Maliro 3:51 - Buku Lopatulika51 Diso langa limvetsa moyo wanga zowawa chifukwa cha ana aakazi onse a m'mzinda mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Diso langa limvetsa moyo wanga zowawa chifukwa cha ana akazi onse a m'mudzi mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Mtima wanga ukupweteka poona zimene zikuŵachitikira akazi a mumzinda mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi chifukwa cha akazi onse a mu mzinda. Onani mutuwo |