Maliro 3:5 - Buku Lopatulika5 Wandimangira zithando za nkhondo, wandizinga ndi ulembe ndi mavuto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wandimangira zithando za nkhondo, wandizinga ndi ulembe ndi mavuto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Adandizinga ndi kundizunguliza ponseponse ndi mazunzo ndi masautso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Wandizinga ndi kundizungulira ndi zowawa ndi zolemetsa. Onani mutuwo |