Maliro 3:41 - Buku Lopatulika41 Titukulire mitima yathu ndi manja athu omwe kwa Mulungu ali kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Titukulire mitima yathu ndi manja athu omwe kwa Mulungu ali kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tikweze mitima yathu ndi manja athu kwa Mulungu kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu kwa Mulungu kumwamba ndipo tinene kuti: Onani mutuwo |