Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:34 - Buku Lopatulika

34 Kupondereza andende onse a m'dziko,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Kupondereza andende onse a m'dziko,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Chauta amadziŵa pamene akulu amapondereza am'ndende am'dziko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Kuphwanya ndi phazi a mʼndende onse a mʼdziko,

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:34
12 Mawu Ofanana  

kuti amve kubuula kwa wandende; namasule ana a imfa.


Pakuti Yehova amvera aumphawi, ndipo sapeputsa am'ndende ake.


Kubuula kwa wandende kufike kuli Inu; monga mwa mphamvu yanu yaikulu lolani ana a imfa atsale.


amene anapululutsa dziko, napasula mizinda yake, amene sanamasule ndende zake, zinke kwao?


ndi kunena kwa iwo amene ali omangidwa, Mukani, kwa iwo amene ali mumdima, Dzionetseni nokha. Iwo adzadya m'njira, ndi m'zitunda zonse zoti see mudzakhala busa lao.


Israele ndiye nkhosa yolowerera, mikango yampirikitsa, poyamba inamudya mfumu ya Asiriya; ndipo pomaliza Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni wathyola mafupa ake.


Pakuti samasautsa dala, ngakhale kumvetsa ana a anthu chisoni.


kupambutsa chiweruzo cha munthu pamaso pa Wam'mwambamwamba;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa