Maliro 3:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo ndinati, Mphamvu yanga yatha, osayembekezanso kanthu kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo ndinati, Mphamvu yanga yatha, osayembekezanso kanthu kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wonse watha, chandithera chikhulupiriro cholandira kanthu ka Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka ndi zonse zimene ndimayembekeza kwa Yehova.” Onani mutuwo |