Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:16 - Buku Lopatulika

16 Wathyolanso mano anga ndi tinsangalabwi, wandikuta ndi phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Wathyolanso mano anga ndi tinsangalabwi, wandikuta ndi phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Adandigulula mano ndi timiyala, adandivimviniza m'phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Wathyola mano anga ndi miyala; wandiviviniza mʼfumbi;

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:16
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anadzitengera phale, kudzikanda nalo; nakhala pansi m'maphulusa.


Kubangula kwa mkango, ndi kulira kwa mkango waukali kwaletsedwa, ndi mano a misona ya mkango athyoledwa.


Pakuti ndadya mapulusa ngati mkate, ndi kusakaniza chomwera changa ndi misozi,


Ukani Yehova; ndipulumutseni, Mulungu wanga! Pakuti mwapanda adani anga onse patsaya; mwawathyola mano oipawo.


Thyolani mano ao m'kamwa mwao, Mulungu, zulani zitsakano za misona ya mkango, Yehova.


Zakudya za chinyengo zikondweretsa munthu; koma pambuyo pake m'kamwa mwake mudzadzala tinsangalabwi.


Iwe mwana wamkazi wa anthu anga, udziveke ndi chiguduli, ndi kumvimvinika m'phulusa; ulire maliro ngati a mwana wamwamuna wa yekha, kulira kowawa koposa; pakuti wakufunkha adzatifikira ife motidzidzimutsa.


Pakuti mau awa anafikira mfumu ya Ninive, ndipo inanyamuka kumpando wake wachifumu, nivula chofunda chake, nifunda chiguduli, nikhala m'maphulusa.


Kapena munthu ndani wa inu, amene pompempha mwana wake mkate, adzampatsa mwala?


Ndipo ndani wa inu ali atate, mwana wake akadzampempha mkate, adzampatsa mwala? Kapena nsomba, nadzamninkha njoka m'malo mwa nsomba?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa