Maliro 3:16 - Buku Lopatulika16 Wathyolanso mano anga ndi tinsangalabwi, wandikuta ndi phulusa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Wathyolanso mano anga ndi tinsangalabwi, wandikuta ndi phulusa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Adandigulula mano ndi timiyala, adandivimviniza m'phulusa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Wathyola mano anga ndi miyala; wandiviviniza mʼfumbi; Onani mutuwo |