Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:12 - Buku Lopatulika

12 Wathifula uta wake, nandiyesa polozetsa muvi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Wathifula uta wake, nandiyesa polozetsa muvi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Adakoka uta wake nandiyesa chinthu chochitirapo chandamale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Wakoka uta wake ndipo walunjikitsa mivi yake pa ine.

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:12
6 Mawu Ofanana  

Pakuti mivi ya Wamphamvuyonse yandilowa, mzimu wanga uwumwa ulembe wake; zoopsa za Mulungu zindindandira nkhondo.


Ngati ndachimwa, ndingachitire Inu chiyani, Inu wodikira anthu? Mwandiikiranji ndikhale chandamali chanu? Kuti ndikhale kwa ine ndekha katundu?


Pakuti mivi yanu yandilowa, ndi dzanja lanu landigwera.


Wathifula uta wake ngati mdani, waima ndi dzanja lake lamanja ngati mmaliwongo; wapha onse okondweretsa maso; watsanulira ukali wake ngati moto pahema wa mwana wamkazi wa Ziyoni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa