Maliro 3:11 - Buku Lopatulika11 Wapambutsa njira zanga, nanding'amba; nandipululutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Wapambutsa njira zanga, nanding'amba; nandipululutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adandisiyitsa njira nanding'ambang'amba, kenaka nkundisiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba, ndipo wandisiya wopanda thandizo. Onani mutuwo |