Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Maliro 3:10 - Buku Lopatulika

10 Andikhalira chilombo cholalira kapena mkango mobisalira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Andikhalira chilombo cholalira kapena mkango mobisalira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Adandiwukira ngati chimbalangondo kapena ngati mkango wondilalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Wandidikirira ngati chimbalangondo, wandibisalira ngati mkango.

Onani mutuwo Koperani




Maliro 3:10
10 Mawu Ofanana  

Ndipo mutu wanga ukadzikweza, mundisaka ngati mkango; mubweranso ndi kudzionetsera modabwitsa kwa ine.


Alalira monga mkango m'ngaka mwake; alalira kugwira wozunzika, agwira wozunzika, pakumkola mu ukonde mwake.


Afanana ndi mkango wofuna kumwetula, ndi msona wa mkango wakukhala mobisalamo.


Ndinadzitonthoza kufikira mamawa; monga mkango, momwemo Iye anathyolathyola mafupa anga onse; Kuyambira usana kufikira usiku mudzanditsiriza ine.


Wapambutsa njira zanga, nanding'amba; nandipululutsa.


Watsekereza njira zanga ndi miyala yosema, nakhotetsa mayendedwe anga.


Pakuti ndidzakhala kwa Efuremu ngati mkango, ndi kwa nyumba ya Yuda ngati msona wa mkango; ndidzamwetula Ine ndi kuchoka; ndidzanyamula, ndipo palibe wakulanditsa.


Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa